Dziko Lonse Likulira: Papa Francis Wamwalira

Image
Lero dziko lonse likulirira. Mtumiki wathu, mtumwi wa mtendere, mtsogoleri wa Tchalitchi cha Katolika Papa Francis   wamwalira ali ndi zaka 88 . Nkhaniyi yatsimikizidwa ndi Vatican m'mawa uno, ndipo ikufalikira mofulumira padziko lonse lapansi. Papa Francis  Papa Francis, anabadwa ngati Jorge Mario Bergoglio ku Argentina, anali Papa woyamba kuchokera ku America, komanso wa mtundu wa Jesuit. Kuyambira atasankhidwa mu March 2013 , anasankha dzina Francis osati chifukwa chokopa, koma kuti akhale ngati Mtumiki wa osauka St. Francis of Assisi . Sanali Papa wa mphamvu anali Papa wa mtima . Anakana kukhala m'nyumba zokongola za Vatican, ndipo anasankha kukhala m'chipinda chaching'ono chisonyezo cha moyo wake wopanda kudzikuza. Papa Francis anali wolimba mtima. Anayankhula za kusintha kwa nyengo (climate change), kusasiyana kwa olemera ndi osauka, kulandira othawa kwawo, komanso za chikondi cha Mulungu kwa aliyense – ngakhale amene ena amawawona ngati osayenera. Anati: “...

Lilongwe City Council Restricts DPP Whistle-Stop Tour Ahead of Official Campaign Period

 

In a move that has stirred political discussion, the Lilongwe City Council (LCC) has turned down the Democratic Progressive Party’s (DPP) request to conduct a whistle-stop tour across multiple locations in Lilongwe City’s Masintha Constituency.

Letter from Lilongwe city council 

The DPP had sought clearance to hold brief rallies at Chilinde, Chiwoko, Matchansi, Biwi, Mchesi, and Kawale this Saturday, starting from 10 a.m. However, in an official response letter seen by this blog, the council has advised the party to select only one location for their rally instead of touring multiple sites.

According to the LCC, the restriction stems from the fact that the official campaign period has not yet begun. The council emphasized that holding rallies in several areas would be contrary to current electoral regulations.

"Since the campaign period hasn't started yet, you are requested to hold a rally in one location. We request your office to formally write us on the place you intend to hold the rally," reads a portion of the council's letter to the DPP.

This development raises questions about how political parties navigate the boundaries between mobilization and campaigning in the pre-campaign season. It also signals increased scrutiny from local authorities as Malawi approaches the heated political season.

It remains to be seen which location the DPP will settle for—and how this decision will shape its outreach strategy moving forward. Stay tuned for updates as the story unfolds.

Comments

Popular posts from this blog

Mfumu Yaikulu Gawa Undi Aletsa Magule Opanda Ulemu pa Kulamba 2025

Ngozi ya Sitima ya M'madzi ku Likoma: Atatu afa, ena asanu ndi atatu apulumutsidwa

Nkhani Yachisoni ku Mchinji: Bambo wamangidwa Atapha Mwana Wake Chifukwa Chosamvera