Dziko Lonse Likulira: Papa Francis Wamwalira

Image
Lero dziko lonse likulirira. Mtumiki wathu, mtumwi wa mtendere, mtsogoleri wa Tchalitchi cha Katolika Papa Francis   wamwalira ali ndi zaka 88 . Nkhaniyi yatsimikizidwa ndi Vatican m'mawa uno, ndipo ikufalikira mofulumira padziko lonse lapansi. Papa Francis  Papa Francis, anabadwa ngati Jorge Mario Bergoglio ku Argentina, anali Papa woyamba kuchokera ku America, komanso wa mtundu wa Jesuit. Kuyambira atasankhidwa mu March 2013 , anasankha dzina Francis osati chifukwa chokopa, koma kuti akhale ngati Mtumiki wa osauka St. Francis of Assisi . Sanali Papa wa mphamvu anali Papa wa mtima . Anakana kukhala m'nyumba zokongola za Vatican, ndipo anasankha kukhala m'chipinda chaching'ono chisonyezo cha moyo wake wopanda kudzikuza. Papa Francis anali wolimba mtima. Anayankhula za kusintha kwa nyengo (climate change), kusasiyana kwa olemera ndi osauka, kulandira othawa kwawo, komanso za chikondi cha Mulungu kwa aliyense – ngakhale amene ena amawawona ngati osayenera. Anati: “...

DR LAZARUS CHAKWERA ASSENTED THE BILLS

 President Lazarus Chakwera has assented to nine bills which were passed by Parliament.


The bills are  Bill No. 22 of 2024: Constitution (Amendment).


Bill No. 23 of 2024: Judicial Service Administration.


Bill No. 25 of 2024: Financial Services (Amendment).


Bill No. 26 of 2024: Insurance.


Bill No. 27 of 2024: Public Procurement and Disposal of Public Assets.


Bill No. 30 of 2024: Value Added Tax (Amendment).


Bill No. 31 of 2024: European Investment Bank (Water Energy Framework) Loan (Authorisation). 


Bill No. 32 of 2024: OPEC Fund for International Development (Shire Valley Transformation Programme Phase II) Authorisation and Ratification).



Bill No. 33 of 2024: Appropriation (Amendment).


This is in line to exercise of the powers vested in him by Section 89 of the Constitution.


State house Press Secretary Anthony Kasunda has confirmed.


“I can confirm that His Excellency has assented to all the Bills which were presented to him by the Office of the Speaker,” Kasunda said.

Comments

Popular posts from this blog

Mfumu Yaikulu Gawa Undi Aletsa Magule Opanda Ulemu pa Kulamba 2025

Ngozi ya Sitima ya M'madzi ku Likoma: Atatu afa, ena asanu ndi atatu apulumutsidwa

Nkhani Yachisoni ku Mchinji: Bambo wamangidwa Atapha Mwana Wake Chifukwa Chosamvera