Dziko Lonse Likulira: Papa Francis Wamwalira

Image
Lero dziko lonse likulirira. Mtumiki wathu, mtumwi wa mtendere, mtsogoleri wa Tchalitchi cha Katolika Papa Francis   wamwalira ali ndi zaka 88 . Nkhaniyi yatsimikizidwa ndi Vatican m'mawa uno, ndipo ikufalikira mofulumira padziko lonse lapansi. Papa Francis  Papa Francis, anabadwa ngati Jorge Mario Bergoglio ku Argentina, anali Papa woyamba kuchokera ku America, komanso wa mtundu wa Jesuit. Kuyambira atasankhidwa mu March 2013 , anasankha dzina Francis osati chifukwa chokopa, koma kuti akhale ngati Mtumiki wa osauka St. Francis of Assisi . Sanali Papa wa mphamvu anali Papa wa mtima . Anakana kukhala m'nyumba zokongola za Vatican, ndipo anasankha kukhala m'chipinda chaching'ono chisonyezo cha moyo wake wopanda kudzikuza. Papa Francis anali wolimba mtima. Anayankhula za kusintha kwa nyengo (climate change), kusasiyana kwa olemera ndi osauka, kulandira othawa kwawo, komanso za chikondi cha Mulungu kwa aliyense – ngakhale amene ena amawawona ngati osayenera. Anati: “...

A 3 YEAR OLD CHILD HAVE DROWN

 A 3-year-old boy child has  drowned in a stagnant water in Balaka, Malawi.


Balaka Police Public Relations Officer Gladson M'bumpha said the incident took place on Tuesday, January 28, 2025 at Kapire Village in Traditional Authority Nsamala in Balaka, Malawi.


M'bumpha identified the child as Happy Loti who went to the neighbour's house to play with his friends.


"The child entered in the neighbours house but within a short period of time, the deceased went out from the house and he did not return until his friends followed him, but found him lying dead in a stagnant water very close to the house" Said M'bumpha 


Balaka District Hospital postmortem examination conducted by the medical practitioner confirmed that the cause of death was due to suffocation, secondary to drowning.


The police is therefore arging the parents to monitor their children whenever they are going to other errands.

Comments

Popular posts from this blog

Mfumu Yaikulu Gawa Undi Aletsa Magule Opanda Ulemu pa Kulamba 2025

Ngozi ya Sitima ya M'madzi ku Likoma: Atatu afa, ena asanu ndi atatu apulumutsidwa

Nkhani Yachisoni ku Mchinji: Bambo wamangidwa Atapha Mwana Wake Chifukwa Chosamvera