Dziko Lonse Likulira: Papa Francis Wamwalira

Image
Lero dziko lonse likulirira. Mtumiki wathu, mtumwi wa mtendere, mtsogoleri wa Tchalitchi cha Katolika Papa Francis   wamwalira ali ndi zaka 88 . Nkhaniyi yatsimikizidwa ndi Vatican m'mawa uno, ndipo ikufalikira mofulumira padziko lonse lapansi. Papa Francis  Papa Francis, anabadwa ngati Jorge Mario Bergoglio ku Argentina, anali Papa woyamba kuchokera ku America, komanso wa mtundu wa Jesuit. Kuyambira atasankhidwa mu March 2013 , anasankha dzina Francis osati chifukwa chokopa, koma kuti akhale ngati Mtumiki wa osauka St. Francis of Assisi . Sanali Papa wa mphamvu anali Papa wa mtima . Anakana kukhala m'nyumba zokongola za Vatican, ndipo anasankha kukhala m'chipinda chaching'ono chisonyezo cha moyo wake wopanda kudzikuza. Papa Francis anali wolimba mtima. Anayankhula za kusintha kwa nyengo (climate change), kusasiyana kwa olemera ndi osauka, kulandira othawa kwawo, komanso za chikondi cha Mulungu kwa aliyense – ngakhale amene ena amawawona ngati osayenera. Anati: “...

PAUL KAGAME TO FIGHT BACK SOUTH AFRICA


Rwandan President Paul Kagame says Rwanda is prepared for a confrontation with South Africa if necessary.

This follows South African President Cyril Ramaphosa’s claim that M23 rebels and Rwanda’s defence force were responsible for the deaths of 13 South African soldiers in the Democratic Republic of Congo (DRC).

Kagame says Ramaphosa had not warned Rwanda about its military activities in the DRC but instead requested logistical support while acknowledging South Africa’s efforts for peace.

Kagame asserted that South Africa is not in a position to act as a peacemaker or mediator and warned that if South Africa seeks confrontation, Rwanda will respond accordingly.

Kagame clarified details of his recent conversations with Ramaphosa, stating, “What has been said about these conversations in the media by South African officials and President Ramaphosa himself contains a lot of distortion, deliberate attacks, and even lies."

"If words can change so much from a conversation to a public statement, it says a lot about how these very important issues are being managed.”

This claims rise after the seculation of images and videos of M23 soldiers and Rwandan soldiers, which are showing similar faces.

Comments

Popular posts from this blog

Mfumu Yaikulu Gawa Undi Aletsa Magule Opanda Ulemu pa Kulamba 2025

Ngozi ya Sitima ya M'madzi ku Likoma: Atatu afa, ena asanu ndi atatu apulumutsidwa

Nkhani Yachisoni ku Mchinji: Bambo wamangidwa Atapha Mwana Wake Chifukwa Chosamvera